TIMU YA FCB NYASA BIG BULLETS YAFIKA MU NDIME YOTSIRIDZA
Timu ya FCB Nyasa Big Bullets yafika mu ndime yotsiridza ya chikho cha Airtel Top 8 itangonjetsa timu ya Karonga United ndi…
Timu ya FCB Nyasa Big Bullets yafika mu ndime yotsiridza ya chikho cha Airtel Top 8 itangonjetsa timu ya Karonga United ndi…
Mtsogoleri wa chipani cha People’s Transformation (Petra) a Kamuzu Walter Chiwambo komanso a Smart Swira omwe ndioima paokha, lero atenga kalata zosonyeza…
Gulu lotchedwa Mangochi-Makanjira Road Concerned Citizens lati lachiwiri pa 24 June, lichita zionetsero zofuna kukakamiza boma kuti likwaniritse lonjezano lake lomanga msewu…
SALIMA ATUMIKIRABE FCB Timu ya mpira wa miyendo ya FCB Nyasa Big , yalengeza kuti Chikumbutso Salima akhala akutumikira ku timuyi mpaka…
Mawanja omwe anavutika ndi ng’amba okwana 13,997 okhala m’madera a Makanjira ndi Lulanga ku Mangochi, akuyembekezeleka kulandira thandizo la chimanga ndi mnthambi…
Timu ya Creck Sporting yachotsa ntchito mphunzitsi wake Joseph Kamwendo ndi omuthandizira Abel Mkandawire komanso Chiukepo Msowoya. Atatuwa achotsedwa kamba ka kusachita…
A Vincent Makida ndiomwe adzaimire ngati phungu wachipani cha MCP. Makida wapambana muzisankho zachipulura ndimavoti 1177 pomwe a Hassan Hussein apeza mavoti…
Bungwe loyendetsa chisankho mdziko muno la MEC lati lichitsa kauniuni wa anthu omwe ali mundandanda ozavota kuyambira lachiwiri sabata yamawa. Bungweli lalengeza…
Mlembi wamkulu ku unduna oona zaubale wamaiko akunja (Foreign Affairs) wati ndiokhutira ndimaphunziro anthumwi zamaiko am’chigawo chakum’mwera kwa Africa (SADC) aukadaulo wamakono…
Bungwe lopelekera magetsi la ESCOM Limited, lati ophunzira achizimayi okwana 120 ndiomwe pakalipano la wathandiza kumaphunziro aukadaulo waluso lamanja ngati mbali imodzi…