MAKIDA NDIYEMWE ANYAMULE MCP KU MANGOCHI.

A Vincent Makida ndiomwe adzaimire ngati phungu wachipani cha MCP.

Makida wapambana muzisankho zachipulura ndimavoti 1177 pomwe a Hassan Hussein apeza mavoti 315 zisankho zomwe zinachitikira pa bwalo la Mangochi stadium.

Related posts

MCP TO HOLD A PRESS BRIEFING AIMED TO SHARPENING THE PARTY’S FUTURE.

MKULU WINA WAPHA BAMBO AKE KAAMBA KAMPUNGA.

BOMA LAPEREKA NDALAMA ZOPOSERA K7 MILLION KUTI ZITHANDIZIRE MWAMBO WAMALIRO KWA MZIKA ZOMWE ZINAFA PANGOZI YA BUS.