Umoyo FM
  • Home
  • Featured
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Lifestyle
  • Sports
  • About Us
  • Contact
  • Login
  • Umoyo FM

    MCP TO HOLD A PRESS BRIEFING AIMED TO SHARPENING THE PARTY’S FUTURE.

    MKULU WINA WAPHA BAMBO AKE KAAMBA KAMPUNGA.

    BOMA LAPEREKA NDALAMA ZOPOSERA K7 MILLION KUTI ZITHANDIZIRE MWAMBO WAMALIRO KWA MZIKA ZOMWE ZINAFA PANGOZI YA BUS.

    NTHAMBI YA ZANKHALANGO YALANDA MATUMBA AMAKALA OKWANA 212 OPANDA CHITUPA.

    Mclove MafutaMay 1, 20250126 views

    Bambo wina wazaka 31 ku Mangochi ali m’manja mwapolisi kaamba kopezeka ndimakala opanda chilolezo. Malinga ndi mneneri wapolisi m’bomali Inspector Amina Tepan…

    Read more

    DZIKO LA MALAWI LIKUYEMBEKEZELEKA KUCHITITSA MSONKHANO WAZAMALIMIDWE WA MAIKO AMUNO MU AFRICA

    Mclove MafutaApril 30, 20250128 views

    Unduna wazamalimidwe walengeza kuti uchititsa msonkhano wachisanu ndi chiwiri (7) wasabata yapadera wamaiko amuno mu Africa(Africa-wide Agricultural Extension Week-AAEW) mwezi wamawa. Nduna…

    Read more

    MTSOGOLERI WAKALE WADZIKO LINO WALENGEZA KUTI AKHALA NAWO PAMWAMBO WAMALIRO MASANA ANO KU BALAKA

    Mclove MafutaApril 10, 20250155 views

    Mtsogoleri wakale wadziko lino Professor Arthur Peter Mutharika yemwenso ndi mtsogoleri wachipani chotsutsa cha Democratic Progressive (DPP) lero akhala nawo pamwambo wamaliro…

    Read more

    Ophunzira wina pa sukulu ya ukachenjede ya DMI ku Mangochi wafa atagundidwa ndi galimoto

    Mclove MafutaApril 8, 20250144 views

    Apolisi ku Mangochi akusunga mchitolokosi shoveli wina wa minbus kaamba kogunda ndikupha ophunzira wapasukulu yaukachenjede ya DMI wazaka 22 usiku wadzulo lolemba…

    Read more

    LERO KUOMBA MPHEPO YOTHAMANGA MAKILOMITA 36 PAOLA ILIYONSE YATERO NTHAMBI YA ZANYENGO.

    Mclove MafutaApril 3, 20250164 views

    Mnthambi yoona zanyengo ndikusintha kwa nyengo (Department of Climate Change and Meteorological Services) yamema anthu okhala m’madera amphepete mwanyanja kuti akhale tcheru…

    Read more

    UNDUNA WAZA UMOYO WAPEMPHA ANTHU KUTENGA NAWO MBALI POKUMBUKIRA MATENDA A ULUMALI OZELEZEKA AMU UBONGO.

    Mclove MafutaApril 2, 20250113 views

    Unduna waza Umoyo mogwirizana ndi bungwe la Autism Hope Trust ndimabungwe ena wati pa 26 mwezi uno uchititsa mwambo okumbukira matenda aulumali…

    Read more

    12 STITCHES PLUS WOUND, LED ESCOM TO DISCLOSE 10 YEAR JAIL TERM CHARGE TO OFFENDER’S

    Mclove MafutaMarch 28, 20250150 views

    The Chief Operations Officer for Electricity Supply Corporation of Malawi (ESCOM) Limited has cautioned the general public that denying assigned staff member’s…

    Read more

    Posts navigation

    1 … 9
    View Desktop Version

    Powered by PenciDesign

    Back To Top