Tilengeza zotsatira m’mawa MEC yatero

Bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) lati lasintha tsiku lochititsira msonkhano wa atolankhani okhudza zotsatira zachisankho.

Mneneli wa bungwe la MEC a Sangwani Mwafulirwa wati bungweli lachita izi kuti lilengeze zotsatira zonse za m’tsogoleri mawa.

A Mwafulirwa alengezanso kuti bungwe la MEC silinalandire chiletso chilichonse lero, kuti asalengeze zotsatirazi

Related posts

MCP TO HOLD A PRESS BRIEFING AIMED TO SHARPENING THE PARTY’S FUTURE.

MKULU WINA WAPHA BAMBO AKE KAAMBA KAMPUNGA.

BOMA LAPEREKA NDALAMA ZOPOSERA K7 MILLION KUTI ZITHANDIZIRE MWAMBO WAMALIRO KWA MZIKA ZOMWE ZINAFA PANGOZI YA BUS.