Umoyo FM
  • Home
  • Featured
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Lifestyle
  • Sports
  • About Us
  • Contact
  • Login
  • Umoyo FM

    https://umoyofm.mw/tigwirizane-polimbana-ndi-hiv/

    TIGWIRIZANE POLIMBANA NDI HIV

    ANTHU APEMPHEDWA KUSINTHA KAGANIZIDWE PA ZAMATENDA OSAPATSIRANA.

    KAMWENDO YAKE YAUMA KU CRECK SPORTING

    Mclove MafutaMay 28, 2025078 views

    Timu ya Creck Sporting yachotsa ntchito mphunzitsi wake Joseph Kamwendo ndi omuthandizira Abel Mkandawire komanso Chiukepo Msowoya. Atatuwa achotsedwa kamba ka kusachita…

    Read more

    MAKIDA NDIYEMWE ANYAMULE MCP KU MANGOCHI.

    Mclove MafutaMay 16, 20250162 views

    A Vincent Makida ndiomwe adzaimire ngati phungu wachipani cha MCP. Makida wapambana muzisankho zachipulura ndimavoti 1177 pomwe a Hassan Hussein apeza mavoti…

    Read more

    BUNGWE LA MEC LALENGEZA KUTI KUYAMBIRA SABATA LA MAWA LIKHALE LIKUCHITITSA KAUNIUNI WA ANTHU OMWE AKUDZAPONYA VOTI.

    Mclove MafutaMay 7, 20250146 views

    Bungwe loyendetsa chisankho mdziko muno la MEC lati lichitsa kauniuni wa anthu omwe ali mundandanda ozavota kuyambira lachiwiri sabata yamawa. Bungweli lalengeza…

    Read more

    MNTHUMWI ZOPOSA 100 ZAPATSIDWA UKADAULO WAMAKONO OYANG’ANIRA CHISANKHO CHAMMAIKO A SADIC

    Mclove MafutaMay 2, 20251102 views

    Mlembi wamkulu ku unduna oona zaubale wamaiko akunja (Foreign Affairs) wati ndiokhutira ndimaphunziro anthumwi zamaiko am’chigawo chakum’mwera kwa Africa (SADC) aukadaulo wamakono…

    Read more

    BUNGWE LA ESCOM LATHANDIZA AMAYI OPOSA 100 KUMAPHUNZIRO AUKADAULO WALUSO LAMANJA.

    Mclove MafutaMay 1, 2025080 views

    Bungwe lopelekera magetsi la ESCOM Limited, lati ophunzira achizimayi okwana 120 ndiomwe pakalipano la wathandiza kumaphunziro aukadaulo waluso lamanja ngati mbali imodzi…

    Read more

    NTHAMBI YA ZANKHALANGO YALANDA MATUMBA AMAKALA OKWANA 212 OPANDA CHITUPA.

    Mclove MafutaMay 1, 2025076 views

    Bambo wina wazaka 31 ku Mangochi ali m’manja mwapolisi kaamba kopezeka ndimakala opanda chilolezo. Malinga ndi mneneri wapolisi m’bomali Inspector Amina Tepan…

    Read more

    DZIKO LA MALAWI LIKUYEMBEKEZELEKA KUCHITITSA MSONKHANO WAZAMALIMIDWE WA MAIKO AMUNO MU AFRICA

    Mclove MafutaApril 30, 2025081 views

    Unduna wazamalimidwe walengeza kuti uchititsa msonkhano wachisanu ndi chiwiri (7) wasabata yapadera wamaiko amuno mu Africa(Africa-wide Agricultural Extension Week-AAEW) mwezi wamawa. Nduna…

    Read more

    MTSOGOLERI WAKALE WADZIKO LINO WALENGEZA KUTI AKHALA NAWO PAMWAMBO WAMALIRO MASANA ANO KU BALAKA

    Mclove MafutaApril 10, 2025089 views

    Mtsogoleri wakale wadziko lino Professor Arthur Peter Mutharika yemwenso ndi mtsogoleri wachipani chotsutsa cha Democratic Progressive (DPP) lero akhala nawo pamwambo wamaliro…

    Read more

    Ophunzira wina pa sukulu ya ukachenjede ya DMI ku Mangochi wafa atagundidwa ndi galimoto

    Mclove MafutaApril 8, 2025085 views

    Apolisi ku Mangochi akusunga mchitolokosi shoveli wina wa minbus kaamba kogunda ndikupha ophunzira wapasukulu yaukachenjede ya DMI wazaka 22 usiku wadzulo lolemba…

    Read more

    LERO KUOMBA MPHEPO YOTHAMANGA MAKILOMITA 36 PAOLA ILIYONSE YATERO NTHAMBI YA ZANYENGO.

    Mclove MafutaApril 3, 20250107 views

    Mnthambi yoona zanyengo ndikusintha kwa nyengo (Department of Climate Change and Meteorological Services) yamema anthu okhala m’madera amphepete mwanyanja kuti akhale tcheru…

    Read more

    Posts navigation

    1 … 7 8
    View Desktop Version

    Powered by PenciDesign

    Back To Top