Umoyo FM
  • Home
  • Featured
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Lifestyle
  • Sports
  • About Us
  • Contact
  • Login
  • Umoyo FM

    ya ulimi

    UMOYOSPORTS

    CHAKWERA WAYAMIKIRA RBM PANTCHITO YABWINO YOMWE IKUGWIRA POBWEDZERETSA CHUMA MDZIKO MUNO.

    Mclove MafutaJuly 18, 20250156 views

    Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus McCathy Chakwera wayamikira bank ya Reserve (RBM) kaamba kochilimika pochepetsa mavuto akusowa kwa ndalama zakunja. Dr Chakwera…

    Read more

    MZIKA ZAPEMPHEDWA KUSANKHA ATSOGOLERI AMASOMPHENYA.

    Mclove MafutaJuly 18, 20250145 views

    Gulu lomwe silandale la Mkamulano wa Yao ku Mangochi, lapempha anthu okhala m’bomali kuti azasankhe phungu yemwe ali ndi mfundo zachitukuko. Wachiwiri…

    Read more

    ANTHU OCHULUKA ATHA OSAVOTA NAWO NGAKHALE ALI MKAUNDULA – CSEIF.

    Mclove MafutaJuly 18, 20250258 views

    Anthu pafupifupi 50,000 ali pachiopsezo choti atha osaponya nawo voti mwezi wa seputembala ngati lamulo silisintha. Wapampando wabungwe la Civil Society Elections…

    Read more

    DPP’s ELECTORAL COMMISSION APPOINTMENT BID HITS SNAG.

    Mclove MafutaJuly 16, 20250170 views

    The Democratic Progressive Party’s (DPP) effort to appoint one of its members, Mackford Somanje, as a commissioner at the Malawi Electoral Commission…

    Read more

    ATSOGOLERI APEMPHEDWA KUTSATIRA MFUNDO ZA DEMOKALASE PAMENE MISONKHANO YOKOPA ANTHU YAYAMBIKA.

    Mclove MafutaJuly 14, 20251351 views

    Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus McCathy Chakwera wapempha anthu kukhala ololerana komanso kulemekeza ufulu wa ena pomwe nyengo ya kampeni yatsegulidwa. Dr…

    Read more

    MAVOTI ADZAWERENGEDWA PAMANJA LATERO BUNGWE LA MEC.

    Mclove MafutaJuly 14, 20250140 views

    Bungwe loyendetsa chisankho mdziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) lalengeza kuti lidzawerengera mavoti pamanja osati pamakina . Mai Justice Annabel Mtalimanja…

    Read more

    KALATA ZOLIMBIRANA MPANDO WA UTSOGOLERI WADZIKO ZOKWANA 17 NDIZO ZATENGEDWA PAKADALIPANO.

    Mclove MafutaJuly 11, 20250229 views

    Mpikisano otenga kalata zosonyeza chidwi chodzapikisana nawo pa mpando wa utsogoleri wadziko muchisankho chapa 16 September ukupitilirabe kukula pomwe lero kalata inanso…

    Read more

    ATSUTSA ZOTI ASILIKALI ANDENDE AKUNYANYALA NTCHITO- PRISON SERVICE.

    Mclove MafutaJuly 11, 20250167 views

    M’nthambi yoona zachitetezo chandende mdziko muno (Malawi Prison Service) yati posatengera mphekesera zoti asilikali ake ali ndi maganizo onyanyala ntchito, chitetezo chinakali…

    Read more

    MEC – LOLEMBA IKHADZIKITSA MWAMBO WAMASIKU OKOPA ANTHU.

    Mclove MafutaJuly 10, 20250170 views

    Bungwe loyendetsa chisankho mdziko muno la MEC lalengeza kuti lolemba pa 14 July, lichititsa mwambo waukulu okhadzikitsa masiku amisonkhano yomwe cholinga chake…

    Read more

    GOVERNMENT TO REHABILITATE A MULTI-BILLION KWACHA IRRIGATION SCHEME IN NKHATA BAY DISTRICT.

    Mclove MafutaJuly 10, 20250196 views

    The Malawi government on Wednesday, has launched rehabilitation works for the 700-hectare Lweya Irrigation Scheme in Nkhata Bay District. Speaking to URS…

    Read more

    Posts navigation

    1 … 6 … 9
    View Desktop Version

    Powered by PenciDesign

    Back To Top