Umoyo FM
  • Home
  • Featured
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Lifestyle
  • Sports
  • About Us
  • Contact
  • Login
  • Umoyo FM

    MCP TO HOLD A PRESS BRIEFING AIMED TO SHARPENING THE PARTY’S FUTURE.

    MKULU WINA WAPHA BAMBO AKE KAAMBA KAMPUNGA.

    BOMA LAPEREKA NDALAMA ZOPOSERA K7 MILLION KUTI ZITHANDIZIRE MWAMBO WAMALIRO KWA MZIKA ZOMWE ZINAFA PANGOZI YA BUS.

    YEMWE AKUDZAPIKISANA NAWO PAMPANDO WAPHUNGU M’DERA LA MANGOCHI MUNICIPAL WAYAMBA NTCHITO YOMANGA ZIPATALA ZING’ONOZING’ONO

    Mclove MafutaAugust 27, 20250363 views

    Pofuna kuchepetsa kuthinana kwa anthu ofuna thandizo pachipatala chachikulu chaboma la Mangochi,a Idi Kalosi omwe akudzapikisana nawo pampando waphungu m’dera la Mangochi…

    Read more

    BANJA LINA ALINJATA LITAPEZEKA NDI MFUTI YOPANDA CHILOLEZO.

    Mclove MafutaJuly 18, 20250140 views

    Banja lina lili m’manja mwa apolisi ku Chiponde m’boma la Mangochi atalipeza ndi mfuti yamtundu wa Pistol yopanda chilolezo. Malingana ndi mneneri…

    Read more

    CHAKWERA WAYAMIKIRA RBM PANTCHITO YABWINO YOMWE IKUGWIRA POBWEDZERETSA CHUMA MDZIKO MUNO.

    Mclove MafutaJuly 18, 20250145 views

    Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus McCathy Chakwera wayamikira bank ya Reserve (RBM) kaamba kochilimika pochepetsa mavuto akusowa kwa ndalama zakunja. Dr Chakwera…

    Read more

    MZIKA ZAPEMPHEDWA KUSANKHA ATSOGOLERI AMASOMPHENYA.

    Mclove MafutaJuly 18, 20250137 views

    Gulu lomwe silandale la Mkamulano wa Yao ku Mangochi, lapempha anthu okhala m’bomali kuti azasankhe phungu yemwe ali ndi mfundo zachitukuko. Wachiwiri…

    Read more

    ANTHU OCHULUKA ATHA OSAVOTA NAWO NGAKHALE ALI MKAUNDULA – CSEIF.

    Mclove MafutaJuly 18, 20250235 views

    Anthu pafupifupi 50,000 ali pachiopsezo choti atha osaponya nawo voti mwezi wa seputembala ngati lamulo silisintha. Wapampando wabungwe la Civil Society Elections…

    Read more

    DPP’s ELECTORAL COMMISSION APPOINTMENT BID HITS SNAG.

    Mclove MafutaJuly 16, 20250155 views

    The Democratic Progressive Party’s (DPP) effort to appoint one of its members, Mackford Somanje, as a commissioner at the Malawi Electoral Commission…

    Read more

    ATSOGOLERI APEMPHEDWA KUTSATIRA MFUNDO ZA DEMOKALASE PAMENE MISONKHANO YOKOPA ANTHU YAYAMBIKA.

    Mclove MafutaJuly 14, 20251316 views

    Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus McCathy Chakwera wapempha anthu kukhala ololerana komanso kulemekeza ufulu wa ena pomwe nyengo ya kampeni yatsegulidwa. Dr…

    Read more

    MAVOTI ADZAWERENGEDWA PAMANJA LATERO BUNGWE LA MEC.

    Mclove MafutaJuly 14, 20250127 views

    Bungwe loyendetsa chisankho mdziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) lalengeza kuti lidzawerengera mavoti pamanja osati pamakina . Mai Justice Annabel Mtalimanja…

    Read more

    KALATA ZOLIMBIRANA MPANDO WA UTSOGOLERI WADZIKO ZOKWANA 17 NDIZO ZATENGEDWA PAKADALIPANO.

    Mclove MafutaJuly 11, 20250184 views

    Mpikisano otenga kalata zosonyeza chidwi chodzapikisana nawo pa mpando wa utsogoleri wadziko muchisankho chapa 16 September ukupitilirabe kukula pomwe lero kalata inanso…

    Read more

    ATSUTSA ZOTI ASILIKALI ANDENDE AKUNYANYALA NTCHITO- PRISON SERVICE.

    Mclove MafutaJuly 11, 20250152 views

    M’nthambi yoona zachitetezo chandende mdziko muno (Malawi Prison Service) yati posatengera mphekesera zoti asilikali ake ali ndi maganizo onyanyala ntchito, chitetezo chinakali…

    Read more

    Posts navigation

    1 … 6 … 9
    View Desktop Version

    Powered by PenciDesign

    Back To Top