Tilengeza zotsatira m’mawa MEC yatero

Bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) lati lasintha tsiku lochititsira msonkhano wa atolankhani okhudza zotsatira zachisankho.

Mneneli wa bungwe la MEC a Sangwani Mwafulirwa wati bungweli lachita izi kuti lilengeze zotsatira zonse za m’tsogoleri mawa.

A Mwafulirwa alengezanso kuti bungwe la MEC silinalandire chiletso chilichonse lero, kuti asalengeze zotsatirazi

Related posts

https://umoyofm.mw/tigwirizane-polimbana-ndi-hiv/

TIGWIRIZANE POLIMBANA NDI HIV

ANTHU APEMPHEDWA KUSINTHA KAGANIZIDWE PA ZAMATENDA OSAPATSIRANA.