Home Uncategorized OFESI ZATSOPANO ZAKHONSOLO YA THYOLO ZATSEGULIDWA.

OFESI ZATSOPANO ZAKHONSOLO YA THYOLO ZATSEGULIDWA.

by Mclove Mafuta
0 comments

Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera lero watsegulira ofesi zatsopano zakhonsolo ya boma la Thyolo yomwe yadya ndalama zokwana K7.9m.

Ofesizi zomwe ndizoposa makumi asanu ndiziwiri (70) mukhale mnthambi zonse zaboma zilipansi pakhonsoloyi komwe anthu azitha kupeza thandizo posatha mtunda.

M’mawu awo Dr Chakwera ati boma lawo silikuona mtundu, chikhalidwe, chipembezo kapena dera koma iwo akuthandiza mzika iliyonse yokhala mdziko muno.

Pomaliza Dr Chakwera apempha anthu kukhala ololerana komanso ogwirizana pochita zinthu kuti chitukuko chadziko lino chizimka napita patsogolo.

Pakalipano mtsogoleri wadziko linoyu akuyembekezeleka kukatseguliranso bwalo la zamasewero latsopano m’boma la Zomba.

You may also like

Leave a Comment

Dowa Community Radio is a community-based radio station established in 2020 to be used as a tool of communication in Dowa district and surrounding areas to facilitate issues of Education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, Climate change and environment, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00