Home Uncategorized MNTHUMWI ZOPOSA 100 ZAPATSIDWA UKADAULO WAMAKONO OYANG’ANIRA CHISANKHO CHAMMAIKO A SADIC

MNTHUMWI ZOPOSA 100 ZAPATSIDWA UKADAULO WAMAKONO OYANG’ANIRA CHISANKHO CHAMMAIKO A SADIC

by Mclove Mafuta
1 comment

Mlembi wamkulu ku unduna oona zaubale wamaiko akunja (Foreign Affairs) wati ndiokhutira ndimaphunziro anthumwi zamaiko am’chigawo chakum’mwera kwa Africa (SADC) aukadaulo wamakono oyang’anira chisankho chomwe chichitike maiko am’derali.

Dr Mwayiwawo Polepole auza izi Umoyo Radio Online potha pamaphunziro omwe atha lero pa 2 May omwe anayambira pa 28 April pamalo ogona alendo a Capital Hotel mumzinda wa Lilongwe.

M’mawu ake a Terry Rose omwe ndi mkulu oona zandale ku SADC ati mnthumwi zadziko la Malawi zomwe zikhale zikuyang’anira zisankho zamaiko ena monga Zambia,Tanzania ndi Seychelles zapeza ukadaulo okwana obweretsa anthu osiyana pamodzi.

Maphunzirowa mnthumwi zoposa 100 zochokera kuboma,mabungwe oima paokha komanso oimilira zipani ndiomwe anatenga nawo gawo pamaphunziropa

Wolemba : Diffrey Jonathan Bwanaisa – Mangochi

02/05/25

You may also like

1 comment

Mclove Mafuta May 3, 2025 - 4:24 am

Nice peace

Reply

Leave a Comment

Dowa Community Radio is a community-based radio station established in 2020 to be used as a tool of communication in Dowa district and surrounding areas to facilitate issues of Education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, Climate change and environment, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00